Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 5:41-46 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

41. 4 Ulemu sindiulandira kwa anthu.

42. Koma ndikudziwani inu, kuti mulibe cikondiea Mulungu mwa inu nokha.

43. Ndadza Ine m'dzina la Atate wanga, ndipo simundilandira Ine; akadza wina m'dzina lace la iye mwini, iyeyu mudzamlandira.

44. Mungathe inu bwanji kukhulupira, 5 popeza mulandira ulemu wina kwa mnzace ndipo ulemu wakucokera kwa Mulungu yekha simuufuna?

45. Musayesa kuti Ine ndidzakunenezani inu kwa Atate; 6 pali wakukunenezani, ndiye Mose, amene inu mumtama.

46. Pakuti mukadakhulupirira Mose, mukadakhulupirira Ine; 7 pakuti iyeyu analembera za Ine.

Werengani mutu wathunthu Yohane 5