Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 5:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa ca ici Ayuda anaonjeza kufuna kumupha, si cifukwa ca kuswa dzuwa la Sabata kokha, komatu amaehanso Mulungu Atate wace wa iye yekha; nadziyesera wolingana ndi Mulungu.

Werengani mutu wathunthu Yohane 5

Onani Yohane 5:18 nkhani