Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 4:12-16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

12. kodi muli wamkuru ndi atate wathu Yakobo amene anatipatsa ife citsimeci, namwamo iye yekha, ndi ana ace, ndi zoweta zace?

13. Yesu anayankha nati kwa iye, Yense wakumwako madzi awa adzamvanso Iudzu;

14. koma iye wakumwa madzi amene Ine ndidzampatsa sadzamva ludzu nthawi zonse; koma madzi amene Ine ndidzampatsa adzakhala mwa iye kasupe wa madzi otumphukira ku moyo wosatha.

15. Mkaziyo ananena kwa iye, Ambuye, ndipatseni madzi amene, kuti ndisamve ludzu, kapena ndisadze kuno kudzatunga.

16. Yesu ananena kwa iye, Muka, kamuitane mwamuna wako, nudze kuno.

Werengani mutu wathunthu Yohane 4