Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 20:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yesu ananena naye, Mkazi, uliranji? ufuna yani? Iyeyu poyesa kuti ndiye wakumunda, ananena ndi iye, Mbuye ngati mwamnyamula iye, ndiuzeni kumene mwamuika iye, ndipo ndidzamcotsa.

Werengani mutu wathunthu Yohane 20

Onani Yohane 20:15 nkhani