Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 16:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma zinthu izi ndalankhula ndi inu kuti ikadza nthawi yao, mukakumbukire kuti ndinakuuzani. Koma izi sindinanena kwa inu kuyambira paciyambi, cifukwa ndinali pamodzi ndi inu.

Werengani mutu wathunthu Yohane 16

Onani Yohane 16:4 nkhani