Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 15:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Inu simunandisankha Ine, koma Ine ndinakusankhani inu, ndipo ndinakuikani, kuti mukamuke inu ndi kubala cipatso, ndi kuti cipatso canu cikhale; kuti cimene ciri conse mukapempha Atate m'dzina langa akakupatseni inu.

Werengani mutu wathunthu Yohane 15

Onani Yohane 15:16 nkhani