Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 14:29-31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

29. Ndipo tsopano 8 ndakuuzani cisanacitike, kuti pamene citacitika mukakhulupire.

30. Sindidzalankhulanso zambiri ndi inu, pakuti 9 mkuru wa dziko lapansi adza; ndipo alibe kanthu mwa Ine;

31. koma kuti dziko lapansi lizindikire kuti ndikonda Atate, ndikuti 10 ndicita monga momwe Atate wandilamulira. Nyamukani, tizimuka kucokera kuno.

Werengani mutu wathunthu Yohane 14