Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 14:12-14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

12. Indetu, indetu, ndinena kwa inu, Wokhulupirira Ine, nchito zimene ndicita Ine adzazicitanso iyeyu; ndipo adzacita zoposa izi; cifukwa ndipita Ine kwa Atate.

13. Ndipo cimene ciri conse mukafunse m'dzina langa, ndidzacicita, kuti Atate akalemekezedwe mwa Mwana.

14. Ngati mudzapempha kanthu m'dzina langa, ndidzacita.

Werengani mutu wathunthu Yohane 14