Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 13:33 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tiana, katsala kanthawi ndikhala ndi inu. Mudzandifunafuna Ine; ndipo monga ndinanena kwa Ayuda, kuti kumene ndinkako Ine, inu simungathe kudza, momwemo ndinena kwa inu tsopano.

Werengani mutu wathunthu Yohane 13

Onani Yohane 13:33 nkhani