Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 12:50 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndidziwa kuti lamulo lace liri moyo wosatha; cifukwa cace zimene ndilankhula, monga momwe Atate wanena ndi Ine, momwemo ndilankhula.

Werengani mutu wathunthu Yohane 12

Onani Yohane 12:50 nkhani