40. 4 Wadetsa maso ao, naumitsa mtima wao;Kuti angaone ndi maso, angazindikire ndi mtima,Nangatembenuke,Ndipo ndingawaciritse.
41. 5 Izi anati Yesaya, cifukwa anaona ulemerero wace; nalankhula za iye.
42. Kungakhale kotero, ambiri a mwa akuru anakhulupirira iye; koma 6 cifukwa ca Afarisi sanabvomereza, kuti angaletsedwe m'sunagoge,
43. 7 pakuti anakonda ulemerero wa anthu koposa ulemerero wa Mulungu.