Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 11:56-57 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

56. Pamenepo analikumfuna Yesu, nanena wina ndi mnzace poimirira iwo m'Kacisi, Muyesa bwanji inu, sadzadza kuphwando kodi?

57. Koma ansembe akulu ndi Afarisi adalamulira, kuti, munthu wina akadziwa pokhala iye, aulule, kuti akamgwire iye.

Werengani mutu wathunthu Yohane 11