Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 10:22-26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

22. Koma kunali phwando la kukonzersanso m'Yerusalemu; nyengoyo ndi yacisanu.

23. Ndipo Yesu analikuyendayenda m'Kacisi m'khumbi la Solomo,

24. Pamenepo Ayuda anamzungulira iye, nanena ndi iye, Kufikira liti musfnkhitsa-slnkhitsa moyo wathu? ngati Inu ndinu Kristu, tiuzeni momveka.

25. Yesu anayankha iwo, Ndakuuzani, ndipo simukhulupirira, Nchitozi ndizicita Ine m'dzina la Atate wanga, zimenezi zindicitira umboni.

26. Koma inu simukhulupira, cifukwa simuli a mwa nkhosa zanga.

Werengani mutu wathunthu Yohane 10