Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 1:38 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Yesu anaceuka, napenya iwo alikumtsata, nanena nao, Mufuna ciani? Ndipo anati kwa iye, Rabi (ndiko kunena posandulika, Mphunzitsi), mukhala kuti?

Werengani mutu wathunthu Yohane 1

Onani Yohane 1:38 nkhani