2. Awa anali paciyambi kwa Mulungu,
3. Zonse: zinalengedwa ndi iye; ndipo kopanda iye sikunalengedwa kanthu kali konse kolengedwa,
4. Mwa iye munali moyo; ndi moyowu unali kuunika kwa anthu.
5. Ndipo kuunikaku kunawala mumdima; ndi mdimawu sunakuzindikira.
6. Kunali munthu, wotumidwa ndi Mulungu, dzina lace ndiye Yohane.