Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yakobo 5:4-7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

4. Taonani, mphotho ya anchitowo anasenga m'minda yanu, yosungidwa ndi inu powanyenga, ipfuula; ndipo mapfuulc a osengawo adalowa m'makutu a Ambuye wa makamu.

5. Mwadyerera padziko, ndipo mwacita zokukondweretsani; mwadyetsa mitima yanu m'tsiku lakupha.

6. Munamtsutsa, munapha wolungamayo, iye sakanizainu.

7. Potero, lezani mtima, abale, kufikira kudza kwace kwa Ambuye. Taonani, wolima munda alindira cipatso cofunikatu ca dziko, ndi kuleza mtima naco kufikira cikalandira mvula ya myundo ndi masika,

Werengani mutu wathunthu Yakobo 5