18. Ndipo anapempheranso; ndipo m'mwamba munatsika mvula, ndi dziko lidabala zipatso zace.
19. Abale anga, ngati wina wa inu asocera posiyana ndi coonadi, ndipo ambweza iye mnzace;
20. azindikire, kuti iyeamene abweza wocimwa ku njira yace yosocera adzapulumutsa munthu kwa imfa, ndipo adzabvundikira macimo aunyinji.