Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yakobo 5:18-20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

18. Ndipo anapempheranso; ndipo m'mwamba munatsika mvula, ndi dziko lidabala zipatso zace.

19. Abale anga, ngati wina wa inu asocera posiyana ndi coonadi, ndipo ambweza iye mnzace;

20. azindikire, kuti iyeamene abweza wocimwa ku njira yace yosocera adzapulumutsa munthu kwa imfa, ndipo adzabvundikira macimo aunyinji.

Werengani mutu wathunthu Yakobo 5