Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yakobo 1:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mphatso iri yonse yabwino, ndi cininkho ciri conse cangwiro zicokera Kumwamba, zotsika kwa Atate wa mauniko, amene alibe cisanduliko, kapena mthunzi wa citembenukiro.

Werengani mutu wathunthu Yakobo 1

Onani Yakobo 1:17 nkhani