Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yakobo 1:1-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. YAKOBO, kapolo wa Mulungu ndi wa Ambuye Yesu Kristu, kwa mafuko khumi ndi awiri a m'cibalaliko: ndikulankhulani.

2. Muciyese cimwemwe cokha, abale anga, m'mene mukugwa m'mayesero a mitundu mitundu;

3. pozindikira kuti ciyesedwe ca cikhulupiriro canu cicita cipiriro.

4. Koma cipiriro cikhale nayo nchito yace yangwiro, kuti mukakhale angwiro ndi opanda cirema, osasowa kanthu konse.

5. Koma wina wa inu ikamsowa nzeru, apemphe kwa Mulungu, amene apatsa kwa onse modzala manja, niwosatonza; ndipo adzampatsa iye,

Werengani mutu wathunthu Yakobo 1