9. koma pewa mafunso opusa, ndi mawerengedwe a mibadwo, ndi ndeu, ndi makani a pamalamulo; pakuti sizipindulitsa, ndipo ziri zacabe.
10. Munthu wopatukira cikhulupiriro, utamcenjeza kamodzi ndi kawiri, umkanize,
11. podziwa kuti worereyo wasandulika konse, nacimwa, nakhala wodzitsutsa Yekha.