Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Tito 3:9-11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

9. koma pewa mafunso opusa, ndi mawerengedwe a mibadwo, ndi ndeu, ndi makani a pamalamulo; pakuti sizipindulitsa, ndipo ziri zacabe.

10. Munthu wopatukira cikhulupiriro, utamcenjeza kamodzi ndi kawiri, umkanize,

11. podziwa kuti worereyo wasandulika konse, nacimwa, nakhala wodzitsutsa Yekha.

Werengani mutu wathunthu Tito 3