Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mateyu 6:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene ponse musala kudya, musakhale ndi nkhope yacisoni, ngati onyengawo; pakuti aipitsa nkhope zao, kuti aonekere kwa anthu kuti alimkusala kudya. Indetu ndinena kwa inu, Iwo alandiriratu mphotho zao.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 6

Onani Mateyu 6:16 nkhani