Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mateyu 5:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

koma Ine ndinena kwa inu, kuti yense wokwiyira mbale wace wopanda cifukwa adzakhala wopalamula mlandu; ndipo amene adzanena ndi mbale wace, Wopanda pace iwe, adzakhala wopalamula mlandu wa akuru: koma amene adzati, Citsiru iwe: adzakhala wopalamula gehena wamoto.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 5

Onani Mateyu 5:22 nkhani