Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mateyu 28:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo popita dzuwa la Sabata, mbanda kuca, tsiku lakuyamba la sabata, anadza Mariya wa Magadala, ndi Mariya winayo, kudzaona manda.

2. Ndipo onani, panali cibvomezi cacikuru; pakuti mngelo wa Ambuye anatsika Kumwamba, nafika kukunkhuniza mwalawo, nakhala pamwamba pace.

3. Kuonekera kwace kunali ngati mphezi, ndi cobvala cace coyeretsa ngati matalala;

4. ndipo ndi kuopsa kwace alondawo ananthunthumira, nakhala ngati anthu akufa.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 28