Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mateyu 26:47 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Iye ali cilankhulire, onani, Yudase, mmodzi wa khumi ndi awiriwo, anadza, ndi pamodzi ndi iye khamu lalikuru la anthu, ndi malupanga ndi mikunkhu, kucokera kwa ansembe akuru ndi akuru a anthu.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 26

Onani Mateyu 26:47 nkhani