Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mateyu 25:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo wa ndalama ziwiriyo anadzanso, nati, Mbuye, munandipatsa ine ndalama ziwiri; onani, ndapindulapo ndalama zina ziwiri.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 25

Onani Mateyu 25:22 nkhani