Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mateyu 24:30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo pomwepo padzaoneka m'thambo cizindikiro ca Mwana wa munthu; ndipo mitundu yonse ya pa dziko lapansi idzadziguguda pacifuwa, nidzapenya Mwana wa munthu alinkudza pa mitambo ya kumwamba, ndi mphamvu ndi ulemerero waukuru.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 24

Onani Mateyu 24:30 nkhani