Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mateyu 23:37 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ha, Yerusalemu, Yerusalemu, amene umapha aneneri, ndi kuwaponya miyala iwo otumidwa kwa iwe! Ine ndinafuna kangati kusonkhanitsa pamodzi ana ako, inde monga thadzi lisonkhanitsa anapiye ace m'mapiko ace, koma inu simunafuna ai!

Werengani mutu wathunthu Mateyu 23

Onani Mateyu 23:37 nkhani