Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mateyu 22:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pomwepo anatumizanso akapolo ena, nanena, Uzani oitanidwawo, Onani, ndakonza phwando langa; ng'ombe zanga, ndi zonona ndinazipha, ndi zinthu zonse zapsya: idzani kuukwati.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 22

Onani Mateyu 22:4 nkhani