Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mateyu 22:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anatumiza kwa Iye ophunzira ao, pamodzi ndi Aherode, amene ananena, Mphunzitsi, tidziwa kuti muli woona, ndipo muphunzitsa njira ya Mulungu moona ndithu, ndipo simusamala munthu ali yense; pakuti simuyang'anira pa nkhope ya anthu.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 22

Onani Mateyu 22:16 nkhani