Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mateyu 18:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ngati mbale wako akucimwira iwe, pita, numlangize pa nokha iwe ndi iye; ngati akumvera iwe, wambweza mbale wako.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 18

Onani Mateyu 18:15 nkhani