Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mateyu 17:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Iye anabvomera, Apereka, Ndipo polowa iye m'nyumba, Yesu anatsogola kunena naye, nati, Simoni, uganiza bwanji? mafumu a dziko lapansi alandira msonkho kwa yani? kwa ana ao kodi, kapena kwa akunja?

Werengani mutu wathunthu Mateyu 17

Onani Mateyu 17:25 nkhani