Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mateyu 17:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Iye ananena kwa iwo, Cifukwa cikhulupiriro canu ncacing'ono: pakuti indetu ndinena kwa inu, Mukakhala naco cikhulupiriro monga kambeu kampiru, mudzati ndi phiri ili, Senderapo umuke kuja; ndipo lidzasendera; ndipo palibe kanthu kadzakulakani kosacitika. [

Werengani mutu wathunthu Mateyu 17

Onani Mateyu 17:20 nkhani