Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 9:34-36 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

34. Koma iwo anakhala cete; pakuti anatsutsana wina ndi mnzace panjira, kuti, wamkuru ndani?

35. Ndipo m'mene anakhala pansi anaitana khumi ndi awiriwo; nanena nao, Ngati munthu afuna kukhala woyamba, akhale wakuthungo wa onse, ndi mtumiki wa onse.

36. Ndipo anatenga kamwana, nakaika pakati pao, nakayangata, nanena nao,

Werengani mutu wathunthu Marko 9