Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 8:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anamgwira dzanja munthu wakhunguyo, naturukira naye kunja kwa mudzi; ndipo atamthira malobvu m'maso mwace, naika manja pa iye, anamfunsa, Uona kanthu kodi?

Werengani mutu wathunthu Marko 8

Onani Marko 8:23 nkhani