Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 8:13-16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

13. Ndipo anawasiya iwo, nalowanso m'ngalawa, nacoka kunka ku tsidya lija.

14. Ndipo ophunzira adaiwala kutenga mikate, ndipo analibe mkate m'ngalawa koma umodzi wokha.

15. Ndipo Iye anawalamula, nanena, Yang'anirani, penyani kuti mupewe cotupitsa mkate ca Afarisi, ndi cotupitsa mkate ca Herode.

16. Ndipo anatsutsana wina ndi mnzace, nanena kuti, Tiribe mikate.

Werengani mutu wathunthu Marko 8