Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 6:51-56 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

51. Ndipo Iye anakwera, nalowa kwa iwo m'ngalawa, ndipo mphepo inaleka; ndipo anadabwa kwakukuru mwa iwo okha;

52. pakuti sanazindikira za mikateyo, kama mitima yao inauma.

53. Ndipo ataoloka iwo, anafika pamtunda ku Genesarete, nakoceza padooko.

54. Ndipo pamene anaturuka m'ngalawa anamzindikila pomwepo,

55. nathamangira dziko lonselo nayamba kunyamula anthu odwaia pa akama ao, kufika nao kumene anamva kuti analiko Iye.

56. Ndipo kumene konse adalowa Iye m'midzi, kapena m'mizinda, kapena m'miraga, anthu anagoneka odwala pamisika, 1 nampempha Iye kuti akakhudze ngakhale mphonje yokha ya cobvala cace; ndipo onse amene anamkhudza anaciritsidwa.

Werengani mutu wathunthu Marko 6