Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 6:40-43 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

40. Ndipo anakhala pansi mabungwe mabungwe a makumi khumi, ndi a makumi asanu.

41. Ndipo Iye anatenga mikate isanuyo ndi nsomba ziwirizo nayang'anakumwamba, nadalitsa, nagawa mikate; napatsa kwa ophunzira kuti apereke kwa iwo; ndi nsomba ziwiri anagawira onsewo.

42. Ndipo anadya iwo onse, nakhuta.

43. Ndipo anatola makombo mitanga khumi ndi iwiri, ndiponso za nsomba.

Werengani mutu wathunthu Marko 6