Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 6:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

pakuti Herode anaopa Yohane, podziwa kuti ali munthu wolungama ndi woyera mtima, ndipo anamsunga iye. Ndipo pamene anamva iye anathedwa nzeru, oakondwa kumva iye.

Werengani mutu wathunthu Marko 6

Onani Marko 6:20 nkhani