6. ndipo litakwera dzuwa zinapserera; ndipo popeza zinalibe mizu zinakhwinyata.
7. Ndipo zina zinagwa paminga, ndipominga inakula, nizitsamwitsa, ndipo sizinabala zipatso.
8. Ndipo zina zinagwa m'nthaka yabwino, ndipo zinapatsa zipatso, ndi kukula ndi kucuruka; ndipo zinabala kupindula makumi atatu, ndi makumi asanundi limodzi, ndi makumi khumi.
9. Ndipo ananena, Amene ali nao makutu akumva amve.