Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 4:6-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. ndipo litakwera dzuwa zinapserera; ndipo popeza zinalibe mizu zinakhwinyata.

7. Ndipo zina zinagwa paminga, ndipominga inakula, nizitsamwitsa, ndipo sizinabala zipatso.

8. Ndipo zina zinagwa m'nthaka yabwino, ndipo zinapatsa zipatso, ndi kukula ndi kucuruka; ndipo zinabala kupindula makumi atatu, ndi makumi asanundi limodzi, ndi makumi khumi.

9. Ndipo ananena, Amene ali nao makutu akumva amve.

Werengani mutu wathunthu Marko 4