Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 4:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo anayambanso kuphunzitsa pambali pa nyanja, Ndipo anasonkhana kwa Iye khamu lalikurukuru, kotero kuti analowa Iye mungalawa, nakhala m'nyanja; ndipo khamu lonse linakhala pamtunda m'mbali mwa nyanja.

2. Ndipo anawaphunzitsa zinthu zambiri m'mafanizo, nanena nao m'ciphunzitso cace,

Werengani mutu wathunthu Marko 4