Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 2:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ananyamuka iye pomwepo, nasenza mphasa, naturuka pamaso pa iwo onse; kotero kuti anadabwa onse, nalemekeza Mulungu, nanena kuti, Zotere sitinaziona ndi kale lonse.

Werengani mutu wathunthu Marko 2

Onani Marko 2:12 nkhani