Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 15:5-12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

5. Koma Yesu sanayankhanso kanthu; kotero kuti Pilato anazizwa.

6. Ndipo adafuwamasulira paphwando wandende mmodzi, amene iwo anampempha,

7. Ndipo analipo wina dzina lace Baraba, womangidwa pamodzi ndi opanduka, amene anapha munthu mumphandumo.

8. Ndipo khamu la anthu anabwera nayamba kupempha kuti acite monga adafuwacitira.

9. Ndipo Pilato anawayankha, nanena nao, Kodi mufuna kuti ndikumasulireni Mfumu ya Ayuda?

10. Pakuti anazindikira kuti ansembe akuru anampereka Iye mwanjiru.

11. Koma ansembe akuru anasonkezera khamulo, kuti makamaka awamasulire Baraba.

12. Ndipo Pilato anawayankhanso, nati kwa iwo, Pamenepo ndidzacita ciani ndi Iye amene mumchula Mfumu ya Ayuda?

Werengani mutu wathunthu Marko 15