Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 15:3-7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Ndipo ansembe akuru anamnenera Iye zinthu zambiri.

4. Ndipo Pilato anamfunsanso, nanena, Suyankha kanthu kodi? taona, akunenera Iwe zinthu zambiri zotere.

5. Koma Yesu sanayankhanso kanthu; kotero kuti Pilato anazizwa.

6. Ndipo adafuwamasulira paphwando wandende mmodzi, amene iwo anampempha,

7. Ndipo analipo wina dzina lace Baraba, womangidwa pamodzi ndi opanduka, amene anapha munthu mumphandumo.

Werengani mutu wathunthu Marko 15