3. Ndipo ansembe akuru anamnenera Iye zinthu zambiri.
4. Ndipo Pilato anamfunsanso, nanena, Suyankha kanthu kodi? taona, akunenera Iwe zinthu zambiri zotere.
5. Koma Yesu sanayankhanso kanthu; kotero kuti Pilato anazizwa.
6. Ndipo adafuwamasulira paphwando wandende mmodzi, amene iwo anampempha,
7. Ndipo analipo wina dzina lace Baraba, womangidwa pamodzi ndi opanduka, amene anapha munthu mumphandumo.