Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 14:72 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pomwepo tambala analira kaciwiri. Ndipo Petro anakumbukila umo Yesu anati kwa iye, kuti, Tambala asanalire kawiri udzandikana katatu. Ndipo pakuganizira ici analira misozi.

Werengani mutu wathunthu Marko 14

Onani Marko 14:72 nkhani