Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 13:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene adzapita nanu kumlandu, nadzakuperekani, musada nkhawa usanayambe mrandu ndi cimene mudzalankhula; koma ci mene cidzapatsidwa kwa inu m'mphindi yomweyo, mucilankhule; pakuti olankhula si ndinu, koma Mzimu Woyera.

Werengani mutu wathunthu Marko 13

Onani Marko 13:11 nkhani