Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 12:39-42 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

39. ndi kukhala nayo mipando yaulemu m'sunagoge, ndi malo aulemu pamapwando:

40. amenewo alusira nyumba za akazi amasiye, napemphera monyenga mau ambiri; amenewa adzalandira kulanga koposa.

41. Ndipo Iye anakhala pansi pandunji pa mosungiramo zopereka, napenya kuti khamu la anthu alikuponya ndalama mosungiramo; ndipo eni cuma ambiri anaponyamo zambiri.

42. Ndipo anadza mkazi wamasiye waumphawi, ndipo iye anaponyamo tindalama tiwiri tanng'ono tofa kakobiri kamodzi.

Werengani mutu wathunthu Marko 12