Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 10:50-52 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

50. Ndipo iye anataya copfunda cace, nazunzuka, nadza kwa Yesu.

51. Ndipo Yesu anamyankha, nati, Ufuna kuti ndikucitire ciani? Ndipo wakhunguyo anati kwa Iye, Raboni, ndilandire kuona kwanga.

52. Ndipo Yesu anati kwa iye, Muka; cikhulupiriro cako cakupulumutsa iwe. Ndipo pomwepo anapenyanso; namtsata Iye panjira.

Werengani mutu wathunthu Marko 10