Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 10:46 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iwo anafika ku Yeriko; ndipo m'mene Iye analikuturuka m'Yeriko, ndi ophunzira ace, ndi khamu lalikuru la anthu, mwana wa Timeyu, Bartimeyu, wopempha wakhungu, analikukhala pansi m'mbali mwa njira.

Werengani mutu wathunthu Marko 10

Onani Marko 10:46 nkhani