Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 1:41-44 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

41. Ndipo Yesu anagwidwa cifundo, natansa dzanja namkhudza iye, nanena naye, Ndifuna; khala wokonzedwa.

42. Ndipo pomwepo khate linamcoka, ndipo anakonzedwa.

43. Ndipo anamuuzitsa, namturutsa pomwepo,

44. nanena naye, Ona, usati unene kanthu kwa munthu ali yense: koma muka, ukadzionetse kwa wansembe, nupereke pa makonzedwe ako 1 zimene adalamulira Mose, zikhale mboni kwa iwo.

Werengani mutu wathunthu Marko 1