Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 1:11-15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

11. ndipo mau anaturuka m'thambo, Mwana wanga wokondedwa ndiwe, mwa Iwe ndikondwera bwino.

12. Ndipo pomwepo Mzimu anamkangamiza kunka kucipululu.

13. Ndipo anakhala m'cipululu masiku makumi anai woyesedwa ndi Satana; nakhala ndi zirombo, ndipo angelo anamtumikira.

14. Ndipo ataperekedwa Yohane, Yesu anadza ku Galileya, nalalikira uthenga wabwino wa Mulungu,

15. nanena, Nthawi yakwanira, ndipo Ufumu wa Mulungu wayandikira; tembenukani mtima, khulupirirani uthenga wabwino.

Werengani mutu wathunthu Marko 1